Yoweli 3
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Kuweruzidwa kwa Mitundu ya Anthu
3 “Masiku amenewo ndiponso nthawi imeneyo,
nditadzabwezeretsanso Yerusalemu ndi Yuda mʼchimake,
2 ndidzasonkhanitsa anthu a mitundu yonse
ndipo ndidzawabweretsa ku Chigwa cha Yehosafati.
Kumeneko ndidzawaweruza
chifukwa cha cholowa changa, anthu anga Aisraeli,
pakuti anabalalitsa anthu anga pakati pa mitundu ya anthu
ndikugawa dziko langa.
3 Anagawana anthu anga pochita maere
ndipo anyamata anawasinthanitsa ndi akazi achiwerewere;
anagulitsa atsikana chifukwa cha vinyo
kuti iwo amwe.
4 “Kodi tsopano inu a ku Turo ndi Sidoni ndi madera onse a Filisitiya, muli ndi chiyani chotsutsana nane? Kodi mukundibwezera pa zinthu zimene ndakuchitirani? Ngati inu mukundibwezera, Ine ndidzabwezera zochita zanu mofulumira ndi mwachangu pa mitu yanu. 5 Pakuti munatenga siliva ndi golide wanga ndi kupita nacho chuma changa chamtengowapatali ku nyumba zanu zopembedzera mafano. 6 Inu munagulitsa anthu a ku Yuda ndi Yerusalemu kwa Agriki, kuti apite kutali ndi malire a dziko lawo.
7 “Taonani, Ine ndidzawachotsa kumalo kumene munawagulitsako, ndipo ndidzabwezera zimene mwachita pa mitu yanu. 8 Ndidzagulitsa ana anu aamuna ndi ana anu aakazi kwa anthu a ku Yuda, ndipo iwo adzawagulitsa kwa Aseba, mtundu wa anthu okhala kutali.” Yehova wayankhula.
9 Lengezani izi pakati pa anthu a mitundu ina:
Konzekerani nkhondo!
Dzutsani ankhondo amphamvu!
Asilikali onse afike pafupi ndipo ayambe nkhondo.
10 Sulani makasu anu kuti akhale malupanga
ndipo zikwanje zanu zikhale mikondo.
Munthu wofowoka anene kuti,
“Ndine wamphamvu!”
11 Bwerani msanga, inu anthu a mitundu yonse kuchokera ku mbali zonse,
ndipo musonkhane kumeneko.
Tumizani ankhondo anu Yehova!
12 “Mitundu ya anthu idzuke;
ipite ku Chigwa cha Yehosafati,
pakuti kumeneko Ine ndidzakhala
ndikuweruza anthu a mitundu yonse yozungulira.
13 Tengani chikwakwa chodulira tirigu,
pakuti mbewu zakhwima.
Bwerani dzapondeni mphesa,
pakuti mopsinyira mphesa mwadzaza
ndipo mitsuko ikusefukira;
kuyipa kwa anthuwa nʼkwakukulu kwambiri!”
14 Chigulu cha anthu, chigulu cha anthu,
mʼchigwa cha chiweruzo!
Pakuti tsiku la Yehova layandikira
mʼchigwa cha chiweruzo.
15 Dzuwa ndi mwezi zidzadetsedwa,
ndipo nyenyezi sizidzawalanso.
16 Yehova adzabangula kuchokera mu Ziyoni
ndipo mawu ake adzamveka ngati bingu kuchokera mu Yerusalemu;
dziko lapansi ndi thambo zidzagwedezeka.
Koma Yehova adzakhala pothawira pa anthu ake,
linga la anthu a ku Israeli.
Madalitso a Anthu a Mulungu
17 “Pamenepo inu mudzadziwa kuti Ine Yehova Mulungu wanu,
ndimakhala mu Ziyoni, phiri langa lopatulika.
Yerusalemu adzakhala wopatulika;
alendo sadzamuthiranso nkhondo.
18 “Tsiku limenelo mapiri adzachucha vinyo watsopano,
ndipo zitunda zidzayenderera mkaka;
mitsinje yonse ya ku Yuda idzadzaza ndi madzi.
Kasupe adzatumphuka mʼnyumba ya Yehova
ndipo adzathirira Chigwa cha Sitimu.
19 Koma Igupto adzasanduka bwinja,
Edomu adzasanduka chipululu,
chifukwa cha nkhondo imene anathira anthu a ku Yuda
mʼdziko limene anakhetsa magazi a anthu osalakwa.
20 Koma Yuda adzakhala ndi anthu mpaka muyaya
ndi Yerusalemu ku mibadomibado.
21 Kukhetsa magazi kwawo kumene Ine sindinakhululuke
ndidzakhululuka.”
Yehova amakhala mu Ziyoni!
Joel 3
New International Version
The Nations Judged
3 [a]“In those days and at that time,
when I restore the fortunes(A) of Judah(B) and Jerusalem,
2 I will gather(C) all nations
and bring them down to the Valley of Jehoshaphat.[b](D)
There I will put them on trial(E)
for what they did to my inheritance, my people Israel,
because they scattered(F) my people among the nations
and divided up my land.
3 They cast lots(G) for my people
and traded boys for prostitutes;
they sold girls for wine(H) to drink.
4 “Now what have you against me, Tyre and Sidon(I) and all you regions of Philistia?(J) Are you repaying me for something I have done? If you are paying me back, I will swiftly and speedily return on your own heads what you have done.(K) 5 For you took my silver and my gold and carried off my finest treasures to your temples.[c](L) 6 You sold the people of Judah and Jerusalem to the Greeks,(M) that you might send them far from their homeland.
7 “See, I am going to rouse them out of the places to which you sold them,(N) and I will return(O) on your own heads what you have done. 8 I will sell your sons(P) and daughters to the people of Judah,(Q) and they will sell them to the Sabeans,(R) a nation far away.” The Lord has spoken.(S)
9 Proclaim this among the nations:
Prepare for war!(T)
Rouse the warriors!(U)
Let all the fighting men draw near and attack.
10 Beat your plowshares into swords
and your pruning hooks(V) into spears.(W)
Let the weakling(X) say,
“I am strong!”(Y)
11 Come quickly, all you nations from every side,
and assemble(Z) there.
Bring down your warriors,(AA) Lord!
12 “Let the nations be roused;
let them advance into the Valley of Jehoshaphat,(AB)
for there I will sit
to judge(AC) all the nations on every side.
13 Swing the sickle,(AD)
for the harvest(AE) is ripe.
Come, trample the grapes,(AF)
for the winepress(AG) is full
and the vats overflow—
so great is their wickedness!”
14 Multitudes,(AH) multitudes
in the valley(AI) of decision!
For the day of the Lord(AJ) is near
in the valley of decision.(AK)
15 The sun and moon will be darkened,
and the stars no longer shine.(AL)
16 The Lord will roar(AM) from Zion
and thunder from Jerusalem;(AN)
the earth and the heavens will tremble.(AO)
But the Lord will be a refuge(AP) for his people,
a stronghold(AQ) for the people of Israel.
Blessings for God’s People
17 “Then you will know(AR) that I, the Lord your God,(AS)
dwell in Zion,(AT) my holy hill.(AU)
Jerusalem will be holy;(AV)
never again will foreigners invade her.(AW)
18 “In that day the mountains will drip new wine,(AX)
and the hills will flow with milk;(AY)
all the ravines of Judah will run with water.(AZ)
A fountain will flow out of the Lord’s house(BA)
and will water the valley of acacias.[d](BB)
19 But Egypt(BC) will be desolate,
Edom(BD) a desert waste,
because of violence(BE) done to the people of Judah,
in whose land they shed innocent blood.
20 Judah will be inhabited forever(BF)
and Jerusalem through all generations.
21 Shall I leave their innocent blood unavenged?(BG)
No, I will not.(BH)”
The Lord dwells in Zion!(BI)
Joel 3
King James Version
3 For, behold, in those days, and in that time, when I shall bring again the captivity of Judah and Jerusalem,
2 I will also gather all nations, and will bring them down into the valley of Jehoshaphat, and will plead with them there for my people and for my heritage Israel, whom they have scattered among the nations, and parted my land.
3 And they have cast lots for my people; and have given a boy for an harlot, and sold a girl for wine, that they might drink.
4 Yea, and what have ye to do with me, O Tyre, and Zidon, and all the coasts of Palestine? will ye render me a recompence? and if ye recompense me, swiftly and speedily will I return your recompence upon your own head;
5 Because ye have taken my silver and my gold, and have carried into your temples my goodly pleasant things:
6 The children also of Judah and the children of Jerusalem have ye sold unto the Grecians, that ye might remove them far from their border.
7 Behold, I will raise them out of the place whither ye have sold them, and will return your recompence upon your own head:
8 And I will sell your sons and your daughters into the hand of the children of Judah, and they shall sell them to the Sabeans, to a people far off: for the Lord hath spoken it.
9 Proclaim ye this among the Gentiles; Prepare war, wake up the mighty men, let all the men of war draw near; let them come up:
10 Beat your plowshares into swords and your pruninghooks into spears: let the weak say, I am strong.
11 Assemble yourselves, and come, all ye heathen, and gather yourselves together round about: thither cause thy mighty ones to come down, O Lord.
12 Let the heathen be wakened, and come up to the valley of Jehoshaphat: for there will I sit to judge all the heathen round about.
13 Put ye in the sickle, for the harvest is ripe: come, get you down; for the press is full, the fats overflow; for their wickedness is great.
14 Multitudes, multitudes in the valley of decision: for the day of the Lord is near in the valley of decision.
15 The sun and the moon shall be darkened, and the stars shall withdraw their shining.
16 The Lord also shall roar out of Zion, and utter his voice from Jerusalem; and the heavens and the earth shall shake: but the Lord will be the hope of his people, and the strength of the children of Israel.
17 So shall ye know that I am the Lord your God dwelling in Zion, my holy mountain: then shall Jerusalem be holy, and there shall no strangers pass through her any more.
18 And it shall come to pass in that day, that the mountains shall drop down new wine, and the hills shall flow with milk, and all the rivers of Judah shall flow with waters, and a fountain shall come forth out of the house of the Lord, and shall water the valley of Shittim.
19 Egypt shall be a desolation, and Edom shall be a desolate wilderness, for the violence against the children of Judah, because they have shed innocent blood in their land.
20 But Judah shall dwell for ever, and Jerusalem from generation to generation.
21 For I will cleanse their blood that I have not cleansed: for the Lord dwelleth in Zion.
The Word of God in Contemporary Chichewa Copyright © 2002, 2016 by Biblica, Inc.® Used by permission of Biblica, Inc.® All rights reserved worldwide. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Mwini © 2002, 2016 ndi Biblica, Inc.® Kugwiritsa ntchito mwachilolezo. Umwini ndi otetezedwa pa dziko lonse.
Holy Bible, New International Version®, NIV® Copyright ©1973, 1978, 1984, 2011 by Biblica, Inc.® Used by permission. All rights reserved worldwide.
NIV Reverse Interlinear Bible: English to Hebrew and English to Greek. Copyright © 2019 by Zondervan.