Add parallel Print Page Options

Mawu a Yobu

Ndipo Yobu anayankha kuti,

“Zoonadi, ndikudziwa kuti zimenezi ndi zoona.
    Koma munthu angathe bwanji kukhala wolungama pamaso pa Mulungu?
Ngakhale wina atafuna kutsutsana naye,
    Iye sangamuyankhe munthuyo ngakhale mawu amodzi omwe.
Mulungu ndi wa nzeru zambiri ndipo mphamvu zake ndi zochuluka.
    Ndani analimbana naye popanda kupwetekeka?
Iye amasuntha mapiri, mapiriwo osadziwa,
    ndipo amawagubuduza ali wokwiya.
Iye amagwedeza dziko lapansi kulisuntha pamalo pake
    ndipo amanjenjemeretsa mizati yake.
Iye amayankhula ndi dzuwa ndipo siliwala;
    Iyeyo amaphimba kuwala kwa nyenyezi.
Ndi Mulungu yekha amene anayala mayiko akumwamba
    ndipo amayenda pa mafunde a pa nyanja.
Iye ndiye mlengi wa nyenyezi zamlalangʼamba ndi akamwiniatsatana,
    nsangwe ndi kumpotosimpita.
10 Iye amachita zozizwitsa zimene sizimvetsetseka,
    zodabwitsa zimene sizingawerengeke.
11 Akapita pafupi ndi ine sindingathe kumuona;
    akadutsa, sindingathe kumuzindikira.
12 Ngati Iye alanda zinthu, ndani angathe kumuletsa?
    Ndani anganene kwa Iye kuti, ‘Mukuchita chiyani?’
13 Mulungu sabweza mkwiyo wake;
    ngakhale gulu lankhondo la Rahabe linawerama pa mapazi ake.

14 “Nanga ine ndingathe kukangana naye bwanji?
    Ndingawapeze kuti mawu oti nʼkutsutsana naye?
15 Ngakhale nditakhala wosalakwa, sindingamuyankhe;
    ndikanangopempha chifundo kwa woweruza wanga.
16 Ngakhale ndikanamuyitana ndipo Iye ndi kuvomera,
    sindikhulupirira kuti akanamva mawu angawo.
17 Iye akanandikantha ndi mphepo yamkuntho,
    ndipo akanandipweteka popanda chifukwa.
18 Mulungu sakanandilola kuti ndipumenso
    koma akanandichulukitsira zowawa.
19 Tikanena za mphamvu, Iye ndi wamphamvudi!
    Ndipo tikanena za chiweruzo cholungama, ndani angamuzenge mlandu?
20 Ngakhale ndikanakhala wosalakwa, zoyankhula zanga zikananditsutsa;
    ndikanakhala wopanda cholakwa, pakamwa panga pakanandipeza wolakwa.

21 “Ngakhale ine ndili wosalakwa,
    sindidziyenereza ndekha;
    moyo wanga ndimawupeputsa.
22 Zonse nʼzofanana; nʼchifukwa chake ndikuti,
    ‘Iye amawononga anthu osalakwa ndi anthu oyipa omwe.’
23 Pamene mkwapulo ubweretsa imfa yadzidzidzi,
    Iye amaseka tsoka la munthu wosalakwayo.
24 Pamene dziko lagwa mʼmanja mwa anthu oyipa
    Iye amawatseka maso anthu oweruza dzikolo.
    Ngati si Iyeyo, nanga ndani?

25 “Masiku anga ndi othamanga kwambiri kupambana munthu waliwiro;
    masikuwo amapita ine osaonapo zabwino.
26 Amayenda ngati mabwato a njedza pa nyanja,
    ngati mphungu zothamangira nyama zoti zidye.
27 Nʼtanena kuti, ‘Ndidzayiwala madandawulo anga,
    ndidzasintha nkhope yanga ndipo ndidzasekerera,’
28 ndikuopabe mavuto anga onse,
    popeza ndikudziwa kuti simudzavomereza kuti ndine wosalakwa.
29 Popeza ndapezeka kale wolakwa
    ndivutikirenji popanda phindu?
30 Ngakhale nditasamba mʼmadzi oyera kwambiri
    ndi kusamba mʼmanja mwanga ndi sopo,
31 mutha kundiponyabe pa dzala,
    kotero kuti ngakhale zovala zanga zomwe zidzandinyansa.

32 “Mulungu si munthu ngati ine kuti ndithe kumuyankha,
    sindingathe kutsutsana naye mʼbwalo la milandu.
33 Pakanapezeka munthu wina kuti akhale mʼkhalapakati wathu,
    kuti atibweretse ife tonse pamodzi,
34 munthu wina woti achotse ndodo ya Mulungu pa ine
    kuti kuopsa kwake kusandichititsenso mantha!
35 Pamenepo ine ndikanatha kuyankhula mosamuopa Mulunguyo,
    koma monga zililimu, sindingathe.

Job

Then Job replied:

“Indeed, I know that this is true.
    But how can mere mortals prove their innocence before God?(A)
Though they wished to dispute with him,(B)
    they could not answer him one time out of a thousand.(C)
His wisdom(D) is profound, his power is vast.(E)
    Who has resisted(F) him and come out unscathed?(G)
He moves mountains(H) without their knowing it
    and overturns them in his anger.(I)
He shakes the earth(J) from its place
    and makes its pillars tremble.(K)
He speaks to the sun and it does not shine;(L)
    he seals off the light of the stars.(M)
He alone stretches out the heavens(N)
    and treads on the waves of the sea.(O)
He is the Maker(P) of the Bear[a] and Orion,
    the Pleiades and the constellations of the south.(Q)
10 He performs wonders(R) that cannot be fathomed,
    miracles that cannot be counted.(S)
11 When he passes me, I cannot see him;
    when he goes by, I cannot perceive him.(T)
12 If he snatches away, who can stop him?(U)
    Who can say to him, ‘What are you doing?’(V)
13 God does not restrain his anger;(W)
    even the cohorts of Rahab(X) cowered at his feet.

14 “How then can I dispute with him?
    How can I find words to argue with him?(Y)
15 Though I were innocent, I could not answer him;(Z)
    I could only plead(AA) with my Judge(AB) for mercy.(AC)
16 Even if I summoned him and he responded,
    I do not believe he would give me a hearing.(AD)
17 He would crush me(AE) with a storm(AF)
    and multiply(AG) my wounds for no reason.(AH)
18 He would not let me catch my breath
    but would overwhelm me with misery.(AI)
19 If it is a matter of strength, he is mighty!(AJ)
    And if it is a matter of justice, who can challenge him[b]?(AK)
20 Even if I were innocent, my mouth would condemn me;
    if I were blameless, it would pronounce me guilty.(AL)

21 “Although I am blameless,(AM)
    I have no concern for myself;(AN)
    I despise my own life.(AO)
22 It is all the same; that is why I say,
    ‘He destroys both the blameless and the wicked.’(AP)
23 When a scourge(AQ) brings sudden death,
    he mocks the despair of the innocent.(AR)
24 When a land falls into the hands of the wicked,(AS)
    he blindfolds its judges.(AT)
    If it is not he, then who is it?(AU)

25 “My days are swifter than a runner;(AV)
    they fly away without a glimpse of joy.(AW)
26 They skim past(AX) like boats of papyrus,(AY)
    like eagles swooping down on their prey.(AZ)
27 If I say, ‘I will forget my complaint,(BA)
    I will change my expression, and smile,’
28 I still dread(BB) all my sufferings,
    for I know you will not hold me innocent.(BC)
29 Since I am already found guilty,
    why should I struggle in vain?(BD)
30 Even if I washed myself with soap(BE)
    and my hands(BF) with cleansing powder,(BG)
31 you would plunge me into a slime pit(BH)
    so that even my clothes would detest me.(BI)

32 “He is not a mere mortal(BJ) like me that I might answer him,(BK)
    that we might confront each other in court.(BL)
33 If only there were someone to mediate between us,(BM)
    someone to bring us together,(BN)
34 someone to remove God’s rod from me,(BO)
    so that his terror would frighten me no more.(BP)
35 Then I would speak up without fear of him,(BQ)
    but as it now stands with me, I cannot.(BR)

Footnotes

  1. Job 9:9 Or of Leo
  2. Job 9:19 See Septuagint; Hebrew me.

Then Job answered and said,

I know it is so of a truth: but how should man be just with God?

If he will contend with him, he cannot answer him one of a thousand.

He is wise in heart, and mighty in strength: who hath hardened himself against him, and hath prospered?

Which removeth the mountains, and they know not: which overturneth them in his anger.

Which shaketh the earth out of her place, and the pillars thereof tremble.

Which commandeth the sun, and it riseth not; and sealeth up the stars.

Which alone spreadeth out the heavens, and treadeth upon the waves of the sea.

Which maketh Arcturus, Orion, and Pleiades, and the chambers of the south.

10 Which doeth great things past finding out; yea, and wonders without number.

11 Lo, he goeth by me, and I see him not: he passeth on also, but I perceive him not.

12 Behold, he taketh away, who can hinder him? who will say unto him, What doest thou?

13 If God will not withdraw his anger, the proud helpers do stoop under him.

14 How much less shall I answer him, and choose out my words to reason with him?

15 Whom, though I were righteous, yet would I not answer, but I would make supplication to my judge.

16 If I had called, and he had answered me; yet would I not believe that he had hearkened unto my voice.

17 For he breaketh me with a tempest, and multiplieth my wounds without cause.

18 He will not suffer me to take my breath, but filleth me with bitterness.

19 If I speak of strength, lo, he is strong: and if of judgment, who shall set me a time to plead?

20 If I justify myself, mine own mouth shall condemn me: if I say, I am perfect, it shall also prove me perverse.

21 Though I were perfect, yet would I not know my soul: I would despise my life.

22 This is one thing, therefore I said it, He destroyeth the perfect and the wicked.

23 If the scourge slay suddenly, he will laugh at the trial of the innocent.

24 The earth is given into the hand of the wicked: he covereth the faces of the judges thereof; if not, where, and who is he?

25 Now my days are swifter than a post: they flee away, they see no good.

26 They are passed away as the swift ships: as the eagle that hasteth to the prey.

27 If I say, I will forget my complaint, I will leave off my heaviness, and comfort myself:

28 I am afraid of all my sorrows, I know that thou wilt not hold me innocent.

29 If I be wicked, why then labour I in vain?

30 If I wash myself with snow water, and make my hands never so clean;

31 Yet shalt thou plunge me in the ditch, and mine own clothes shall abhor me.

32 For he is not a man, as I am, that I should answer him, and we should come together in judgment.

33 Neither is there any daysman betwixt us, that might lay his hand upon us both.

34 Let him take his rod away from me, and let not his fear terrify me:

35 Then would I speak, and not fear him; but it is not so with me.