Yeremiya 45
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Uthenga kwa Baruki
45 Uwu ndi uthenga umene mneneri Yeremiya anawuza Baruki mwana wa Neriya mʼchaka cha chinayi cha Yehoyakimu mwana wa mwana ya Yosiya kuti alembe mʼbuku. 2 “Yehova Mulungu wa Israeli, akunena kwa iwe Baruki kuti: 3 Iwe unati, ‘Kalanga ine! Yehova wawonjezera chisoni pa mavuto anga. Ine ndatopa ndi kubuwula ndipo sindikupeza mpumulo.’ ”
4 Koma Yehova akukuwuza kuti, “Ndidzagwetsa chimene ndinamanga ndipo ndidzazula chimene ndinadzala. Ndidzachita zimenezi mʼdziko lonse. 5 Kodi tsono ukudzifunira wekha zinthu zazikulu? Usadzifunire. Pakuti ndidzagwetsa mavuto pa anthu onse, koma ndidzasunga moyo wako kulikonse kumene ungadzapite.”
Jeremiah 45
New International Version
A Message to Baruch
45 When Baruch(A) son of Neriah(B) wrote on a scroll(C) the words Jeremiah the prophet dictated in the fourth year of Jehoiakim(D) son of Josiah king of Judah, Jeremiah said this to Baruch: 2 “This is what the Lord, the God of Israel, says to you, Baruch: 3 You said, ‘Woe(E) to me! The Lord has added sorrow(F) to my pain;(G) I am worn out with groaning(H) and find no rest.’(I) 4 But the Lord has told me to say to you, ‘This is what the Lord says: I will overthrow what I have built and uproot(J) what I have planted,(K) throughout the earth.(L) 5 Should you then seek great(M) things for yourself? Do not seek them.(N) For I will bring disaster(O) on all people,(P) declares the Lord, but wherever you go I will let you escape(Q) with your life.’”(R)
The Word of God in Contemporary Chichewa Copyright © 2002, 2016 by Biblica, Inc.® Used by permission of Biblica, Inc.® All rights reserved worldwide. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Mwini © 2002, 2016 ndi Biblica, Inc.® Kugwiritsa ntchito mwachilolezo. Umwini ndi otetezedwa pa dziko lonse.
Holy Bible, New International Version®, NIV® Copyright ©1973, 1978, 1984, 2011 by Biblica, Inc.® Used by permission. All rights reserved worldwide.
NIV Reverse Interlinear Bible: English to Hebrew and English to Greek. Copyright © 2019 by Zondervan.