Add parallel Print Page Options

Salimo la Ana a Kora.

87 Iye wakhazikitsa maziko ake pa phiri loyera;
    Yehova amakonda zipata za Ziyoni
    kupambana malo onse okhalamo a Yakobo.
Za ulemerero wako zimakambidwa,
    Iwe mzinda wa Mulungu:
            Sela
“Ndidzanena za Rahabe ndi Babuloni
    pakati pa iwo amene amandidziwa.
Dzikonso la Filisitiya, Turo pamodzi ndi Kusi,
    ndipo ndidzati, ‘Uyu anabadwira mʼZiyoni.’ ”

Ndithudi, za Ziyoni adzanena kuti,
    “Uyu ndi uyo anabadwira mwa iye,
    ndipo Wammwambamwamba adzakhazikitsa iyeyo.”
Yehova adzalemba mʼbuku la kawundula wa anthu a mitundu ina:
    “Uyu anabadwira mʼZiyoni.”
            Sela
Oyimba ndi ovina omwe adzati,
    “Akasupe anga onse ali mwa iwe.”

Psalm 87

Of the Sons of Korah. A psalm. A song.

He has founded his city on the holy mountain.(A)
The Lord loves the gates of Zion(B)
    more than all the other dwellings of Jacob.

Glorious things are said of you,
    city of God:[a](C)
“I will record Rahab[b](D) and Babylon
    among those who acknowledge me—
Philistia(E) too, and Tyre(F), along with Cush[c]
    and will say, ‘This one was born in Zion.’”[d](G)
Indeed, of Zion it will be said,
    “This one and that one were born in her,
    and the Most High himself will establish her.”
The Lord will write in the register(H) of the peoples:
    “This one was born in Zion.”

As they make music(I) they will sing,
    “All my fountains(J) are in you.”

Footnotes

  1. Psalm 87:3 The Hebrew has Selah (a word of uncertain meaning) here and at the end of verse 6.
  2. Psalm 87:4 A poetic name for Egypt
  3. Psalm 87:4 That is, the upper Nile region
  4. Psalm 87:4 Or “I will record concerning those who acknowledge me: / ‘This one was born in Zion.’ / Hear this, Rahab and Babylon, / and you too, Philistia, Tyre and Cush.”