Add parallel Print Page Options

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa gititi. Salimo la Davide.

Inu Yehova Ambuye athu,
    dzina lanu ndi la lamphamvudi pa dziko lonse lapansi!

Inu mwakhazikitsa ulemerero wanu
    mʼmayiko onse akumwamba.
Kuchokera mʼkamwa mwa ana ndi makanda,
    Inu mwakhazikitsa mphamvu
chifukwa cha adani anu,
    kukhazikitsa bata adani ndi anthu obwezera zoyipa.

Pamene ndilingalira za mayiko anu akumwamba,
    ntchito ya zala zanu,
mwezi ndi nyenyezi,
    zimene mwaziyika pa malo ake,
munthu ndani kuti Inu mumamukumbukira,
    ndi mwana wa munthu kuti inu mumacheza naye?
Inu munamupanga kukhala wocheperapo kusiyana ndi zolengedwa zakumwamba
    ndipo mwamuveka ulemerero ndi ulemu.

Inu munamuyika wolamulira ntchito ya manja anu;
    munayika zinthu zonse pansi pa mapazi ake;
nkhosa, mbuzi ndi ngʼombe pamodzi
    ndi nyama zakuthengo,
mbalame zamlengalenga
    ndi nsomba zamʼnyanja
    zonse zimene zimayenda pansi pa nyanja.

Inu Yehova, Ambuye athu,
    dzina lanu ndi lamphamvudi pa dziko lonse lapansi!

Psalm 8[a]

For the director of music. According to gittith.[b] A psalm of David.

Lord, our Lord,
    how majestic is your name(A) in all the earth!

You have set your glory(B)
    in the heavens.(C)
Through the praise of children and infants
    you have established a stronghold(D) against your enemies,
    to silence the foe(E) and the avenger.
When I consider your heavens,(F)
    the work of your fingers,(G)
the moon and the stars,(H)
    which you have set in place,
what is mankind that you are mindful of them,
    human beings that you care for them?[c](I)

You have made them[d] a little lower than the angels[e](J)
    and crowned them[f] with glory and honor.(K)
You made them rulers(L) over the works of your hands;(M)
    you put everything under their[g] feet:(N)
all flocks and herds,(O)
    and the animals of the wild,(P)
the birds in the sky,
    and the fish in the sea,(Q)
    all that swim the paths of the seas.

Lord, our Lord,
    how majestic is your name in all the earth!(R)

Footnotes

  1. Psalm 8:1 In Hebrew texts 8:1-9 is numbered 8:2-10.
  2. Psalm 8:1 Title: Probably a musical term
  3. Psalm 8:4 Or what is a human being that you are mindful of him, / a son of man that you care for him?
  4. Psalm 8:5 Or him
  5. Psalm 8:5 Or than God
  6. Psalm 8:5 Or him
  7. Psalm 8:6 Or made him ruler . . . ; / . . . his