Add parallel Print Page Options

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Potsata mayimbidwe a “Njiwa pa Mtengo wa Thundu wa Kutali.” Mikitamu ya Davide, pamene Afilisti anamugwira ku Gati.

56 Mundichitire chifundo Inu Mulungu, pakuti anthu akundithamangitsa kwambiri;
    tsiku lonse akundithira nkhondo.
Ondinyoza akundithamangitsa tsiku lonse,
    ambiri akumenyana nane monyada.

Ndikachita mantha
    ndimadalira Inu.
Mwa Mulungu, amene mawu ake ine ndimatamanda,
    mwa Mulungu ine ndimadaliramo; sindidzachita mantha.
    Kodi munthu amene amafa angandichite chiyani?

Tsiku lonse amatembenuza mawu anga;
    nthawi zonse amakonza zondivulaza.
Iwo amakambirana, amandibisalira,
    amayangʼanitsitsa mayendedwe anga
    ndipo amakhala ndi chidwi chofuna kuchotsa moyo wanga.

Musalole konse kuti athawe;
    mu mkwiyo wanu Mulungu mugwetse mitundu ya anthu.
Mulembe za kulira kwanga,
    mulembe chiwerengero cha misozi yanga mʼbuku lanu.
    Kodi zimenezi sizinalembedwe mʼbuku lanulo?

Adani anga adzabwerera mʼmbuyo
    pamene ndidzalirira kwa Inu.
    Pamenepo ndidzadziwa kuti Mulungu ali ku mbali yanga.
10 Mwa Mulungu amene mawu ake ndimawatamanda,
    mwa Yehova amene mawu ake ndimawatamanda,
11 mwa Mulungu ine ndimadalira ndipo sindidzachita mantha.
    Kodi munthu angandichite chiyani?

12 Ndiyenera kuchita zomwe ndinalumbira kwa Mulungu;
    ndidzapereka nsembe zanga zachiyamiko kwa inu.
13 Pakuti mwawombola moyo wanga ku imfa
    ndi mapazi anga kuti ndingagwe,
kuti ndiyende pamaso pa Mulungu
    mʼkuwala kwa moyo.

Psalm 56[a]

For the director of music. To the tune of “A Dove on Distant Oaks.” Of David. A miktam.[b] When the Philistines had seized him in Gath.

Be merciful to me,(A) my God,
    for my enemies are in hot pursuit;(B)
    all day long they press their attack.(C)
My adversaries pursue me all day long;(D)
    in their pride many are attacking me.(E)

When I am afraid,(F) I put my trust in you.(G)
    In God, whose word I praise—(H)
in God I trust and am not afraid.(I)
    What can mere mortals do to me?(J)

All day long they twist my words;(K)
    all their schemes are for my ruin.
They conspire,(L) they lurk,
    they watch my steps,(M)
    hoping to take my life.(N)
Because of their wickedness do not[c] let them escape;(O)
    in your anger, God, bring the nations down.(P)

Record my misery;
    list my tears on your scroll[d](Q)
    are they not in your record?(R)
Then my enemies will turn back(S)
    when I call for help.(T)
    By this I will know that God is for me.(U)

10 In God, whose word I praise,
    in the Lord, whose word I praise—
11 in God I trust and am not afraid.
    What can man do to me?

12 I am under vows(V) to you, my God;
    I will present my thank offerings to you.
13 For you have delivered me from death(W)
    and my feet from stumbling,
that I may walk before God
    in the light of life.(X)

Footnotes

  1. Psalm 56:1 In Hebrew texts 56:1-13 is numbered 56:2-14.
  2. Psalm 56:1 Title: Probably a literary or musical term
  3. Psalm 56:7 Probable reading of the original Hebrew text; Masoretic Text does not have do not.
  4. Psalm 56:8 Or misery; / put my tears in your wineskin

56 Be merciful unto me, O God: for man would swallow me up; he fighting daily oppresseth me.

Mine enemies would daily swallow me up: for they be many that fight against me, O thou most High.

What time I am afraid, I will trust in thee.

In God I will praise his word, in God I have put my trust; I will not fear what flesh can do unto me.

Every day they wrest my words: all their thoughts are against me for evil.

They gather themselves together, they hide themselves, they mark my steps, when they wait for my soul.

Shall they escape by iniquity? in thine anger cast down the people, O God.

Thou tellest my wanderings: put thou my tears into thy bottle: are they not in thy book?

When I cry unto thee, then shall mine enemies turn back: this I know; for God is for me.

10 In God will I praise his word: in the Lord will I praise his word.

11 In God have I put my trust: I will not be afraid what man can do unto me.

12 Thy vows are upon me, O God: I will render praises unto thee.

13 For thou hast delivered my soul from death: wilt not thou deliver my feet from falling, that I may walk before God in the light of the living?