Add parallel Print Page Options

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe wa zida za zingwe. Salimo la Davide.

Ndiyankheni pamene ndiyitana Inu,
    Inu Mulungu wa chilungamo changa.
Pumulitseni ku zowawa zanga;
    chitireni chifundo ndi kumva pemphero langa.

Anthu inu, mpaka liti mudzakhala mukusandutsa ulemerero wanga kukhala manyazi?
    Mpaka liti mudzakonda zachabe ndi kufuna milungu yabodza?
            Sela.
Dziwani kuti Yehova wadziyikira padera anthu okhulupirika;
    Yehova adzamva pamene ndidzamuyitana.

Kwiyani koma musachimwe;
    pamene muli pa mabedi anu,
    santhulani mitima yanu ndi kukhala chete.
            Sela
Perekani nsembe zolungama
    ndipo dalirani Yehova.

Ambiri akufunsa kuti, “Ndani angationetse chabwino chilichonse?”
    Kuwunika kwa nkhope yanu kutiwalire, Inu Yehova.
Inu mwadzaza mtima wanga ndi chimwemwe chachikulu
    kuposa kuchuluka kwa tirigu wawo ndi vinyo watsopano.
Ine ndidzagona ndi kupeza tulo mwamtendere,
    pakuti Inu nokha, Inu Yehova,
    mumandisamalira bwino.

Psalm 4[a]

For the director of music. With stringed instruments. A psalm of David.

Answer me(A) when I call to you,
    my righteous God.
Give me relief from my distress;(B)
    have mercy(C) on me and hear my prayer.(D)

How long will you people turn my glory(E) into shame?(F)
    How long will you love delusions and seek false gods[b]?[c](G)
Know that the Lord has set apart his faithful servant(H) for himself;
    the Lord hears(I) when I call to him.

Tremble and[d] do not sin;(J)
    when you are on your beds,(K)
    search your hearts and be silent.
Offer the sacrifices of the righteous
    and trust in the Lord.(L)

Many, Lord, are asking, “Who will bring us prosperity?”
    Let the light of your face shine on us.(M)
Fill my heart(N) with joy(O)
    when their grain and new wine(P) abound.

In peace(Q) I will lie down and sleep,(R)
    for you alone, Lord,
    make me dwell in safety.(S)

Footnotes

  1. Psalm 4:1 In Hebrew texts 4:1-8 is numbered 4:2-9.
  2. Psalm 4:2 Or seek lies
  3. Psalm 4:2 The Hebrew has Selah (a word of uncertain meaning) here and at the end of verse 4.
  4. Psalm 4:4 Or In your anger (see Septuagint)