Add parallel Print Page Options

Salimo la Davide.

26 Weruzeni Inu Yehova
    pakuti ndakhala moyo wosalakwa.
Ndadalira Yehova
    popanda kugwedezeka.
Patseni mayeso, Inu Yehova ndipo ndiyeseni,
    santhulani mtima wanga ndi maganizo anga;
pakuti chikondi chanu chili pamaso panga nthawi zonse,
    ndipo ndimayenda mʼchoonadi chanu nthawi zonse.
Ine sindikhala pansi pamodzi ndi anthu achinyengo,
    kapena kufunsa nzeru kwa achiphamaso.
Ndimanyansidwa ndi msonkhano wa anthu ochita zoyipa
    ndipo ndimakana kukhala pansi pamodzi ndi oyipa.
Ndimasamba mʼmanja mwanga kuonetsa kusalakwa kwanga
    ndi kupita kukatumikira pa guwa lanu la nsembe, Inu Yehova,
kulengeza mofuwula za matamando anu
    ndi kuwuza onse za ntchito zanu zodabwitsa.
Ndimakonda Nyumba imene Inu Yehova mumakhalamo,
    malo amene ulemerero wanu umapezekako.

Musachotse moyo wanga pamodzi ndi ochimwa,
    moyo wanga pamodzi ndi anthu akupha anzawo,
10 amene mʼmanja mwawo muli ndondomeko zoyipa,
    dzanja lawo lamanja ladzaza ndi ziphuphu.
11 Koma ine ndimakhala moyo wosalakwa;
    mu msonkhano wa anthu anu ndidzatamanda Yehova.

12 Ndayima pa malo wopanda zovuta
    ndipo ndidzatamanda Yehova mu msonkhano waukulu.

Psalm 26

Of David.

Vindicate me,(A) Lord,
    for I have led a blameless life;(B)
I have trusted(C) in the Lord
    and have not faltered.(D)
Test me,(E) Lord, and try me,
    examine my heart and my mind;(F)
for I have always been mindful of your unfailing love(G)
    and have lived(H) in reliance on your faithfulness.(I)

I do not sit(J) with the deceitful,
    nor do I associate with hypocrites.(K)
I abhor(L) the assembly of evildoers
    and refuse to sit with the wicked.
I wash my hands in innocence,(M)
    and go about your altar, Lord,
proclaiming aloud your praise(N)
    and telling of all your wonderful deeds.(O)

Lord, I love(P) the house where you live,
    the place where your glory dwells.(Q)
Do not take away my soul along with sinners,
    my life with those who are bloodthirsty,(R)
10 in whose hands are wicked schemes,(S)
    whose right hands are full of bribes.(T)
11 I lead a blameless life;
    deliver me(U) and be merciful to me.

12 My feet stand on level ground;(V)
    in the great congregation(W) I will praise the Lord.

26 Judge me, O Lord; for I have walked in mine integrity: I have trusted also in the Lord; therefore I shall not slide.

Examine me, O Lord, and prove me; try my reins and my heart.

For thy lovingkindness is before mine eyes: and I have walked in thy truth.

I have not sat with vain persons, neither will I go in with dissemblers.

I have hated the congregation of evil doers; and will not sit with the wicked.

I will wash mine hands in innocency: so will I compass thine altar, O Lord:

That I may publish with the voice of thanksgiving, and tell of all thy wondrous works.

Lord, I have loved the habitation of thy house, and the place where thine honour dwelleth.

Gather not my soul with sinners, nor my life with bloody men:

10 In whose hands is mischief, and their right hand is full of bribes.

11 But as for me, I will walk in mine integrity: redeem me, and be merciful unto me.

12 My foot standeth in an even place: in the congregations will I bless the Lord.