Add parallel Print Page Options

146 Tamandani Yehova.

Tamanda Yehova, iwe moyo wanga.
    Ndidzatamanda Yehova ndi moyo wanga wonse;
    ndidzayimba nyimbo zamatamando kwa Mulungu wanga nthawi yonse ya moyo wanga.

Musamadalire mafumu,
    anthu osakhalitsa, amene sangathe kupulumutsa.
Pamene mizimu yawo yachoka, iwo amabwerera ku dothi;
    zimene ankafuna kuchita zimatha tsiku lomwelo.

Wodala ndi amene thandizo lake ndi
    Mulungu wa Yakobo.
Wolenga kumwamba ndi dziko lapansi,
    nyanja ndi zonse zili mʼmenemo;
    Yehova, amene ndi wokhulupirika kwamuyaya.
Iye amachitira chilungamo anthu oponderezedwa
    ndipo amapereka chakudya kwa anthu anjala.
Yehova amamasula amʼndende,
    Yehova amatsekula maso anthu osaona,
Yehova amadzutsa onse amene awerama pansi,
    Yehova amakonda anthu olungama.
Yehova amasamalira alendo
    ndipo amathandiza ana ndi akazi amasiye,
    koma amasokoneza njira za anthu oyipa.

10 Yehova ndiye Mfumu mpaka muyaya,
    Mulungu wako iwe Ziyoni, pa mibado yonse.

Tamandani Yehova.

Psalm 146

Praise the Lord.[a]

Praise the Lord,(A) my soul.

I will praise the Lord all my life;(B)
    I will sing praise(C) to my God as long as I live.(D)
Do not put your trust in princes,(E)
    in human beings,(F) who cannot save.
When their spirit departs, they return to the ground;(G)
    on that very day their plans come to nothing.(H)
Blessed are those(I) whose help(J) is the God of Jacob,
    whose hope is in the Lord their God.

He is the Maker of heaven(K) and earth,
    the sea, and everything in them—
    he remains faithful(L) forever.
He upholds(M) the cause of the oppressed(N)
    and gives food to the hungry.(O)
The Lord sets prisoners free,(P)
    the Lord gives sight(Q) to the blind,(R)
the Lord lifts up those who are bowed down,(S)
    the Lord loves the righteous.(T)
The Lord watches over the foreigner(U)
    and sustains the fatherless(V) and the widow,(W)
    but he frustrates the ways of the wicked.

10 The Lord reigns(X) forever,
    your God, O Zion, for all generations.

Praise the Lord.

Footnotes

  1. Psalm 146:1 Hebrew Hallelu Yah; also in verse 10