Add parallel Print Page Options

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide.

13 Mpaka liti Yehova? Kodi mudzandiyiwala mpaka kalekale?
    Mpaka liti mudzandibisira nkhope yanu?
Ndidzalimbana ndi maganizo anga
    ndi kukhala ndi chisoni mu mtima mwanga tsiku lililonse mpaka liti?
    Mpaka liti adani anga adzandipambana?

Ndiyangʼaneni ndi kundiyankha, Inu Yehova Mulungu wanga.
    Walitsani maso anga kuti ndingafe;
mdani wanga adzati, “Ndamugonjetsa,”
    ndipo adani anga adzakondwera pamene ine ndagwa.

Koma ndikudalira chikondi chanu chosasinthika;
    mtima wanga umakondwera ndi chipulumutso chanu.
Ine ndidzayimbira Yehova
    pakuti wandichitira zokoma.

Psalm 13[a]

For the director of music. A psalm of David.

How long,(A) Lord? Will you forget me(B) forever?
    How long will you hide your face(C) from me?
How long must I wrestle with my thoughts(D)
    and day after day have sorrow in my heart?
    How long will my enemy triumph over me?(E)

Look on me(F) and answer,(G) Lord my God.
    Give light to my eyes,(H) or I will sleep in death,(I)
and my enemy will say, “I have overcome him,(J)
    and my foes will rejoice when I fall.(K)

But I trust in your unfailing love;(L)
    my heart rejoices in your salvation.(M)
I will sing(N) the Lord’s praise,
    for he has been good to me.

Footnotes

  1. Psalm 13:1 In Hebrew texts 13:1-6 is numbered 13:2-6.