Add parallel Print Page Options

Salimo. Nyimbo yothokoza.

100 Fuwulani kwa Yehova mwachimwemwe, inu dziko lonse lapansi.
    Mulambireni Yehova mosangalala;
    bwerani pamaso pake ndi nyimbo zachikondwerero.
Dziwani kuti Yehova ndi Mulungu.
    Iye ndiye amene anatipanga ndipo ife ndife ake;
    ndife anthu ake, nkhosa za pabusa pake.

Lowani ku zipata zake ndi chiyamiko
    ndi ku mabwalo ake ndi matamando;
    muyamikeni ndi kutamanda dzina lake.
Pakuti Yehova ndi wabwino ndipo chikondi chake ndi chamuyaya;
    kukhulupirika kwake nʼkokhazikika pa mibado ndi mibado.

Psalm 100

A psalm. For giving grateful praise.

Shout for joy(A) to the Lord, all the earth.
    Worship the Lord(B) with gladness;
    come before him(C) with joyful songs.
Know that the Lord is God.(D)
    It is he who made us,(E) and we are his[a];
    we are his people,(F) the sheep of his pasture.(G)

Enter his gates with thanksgiving(H)
    and his courts(I) with praise;
    give thanks to him and praise his name.(J)
For the Lord is good(K) and his love endures forever;(L)
    his faithfulness(M) continues through all generations.

Footnotes

  1. Psalm 100:3 Or and not we ourselves