Malaki 4
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Tsiku la Yehova
4 Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Ndithu tsiku likubwera; lidzayaka ngati ngʼanjo. Anthu onse odzikuza, ndi aliyense ochita zoyipa adzapsa ngati chiputu, ndipo pa tsiku limene likubweralo adzapserera ndi moto. Sipadzatsalira muzu kapena nthambi. 2 Koma inu amene mumaopa dzina langa, dzuwa lachilungamo lidzakutulukirani lili ndi kuwala kokuchiritsani. Ndipo inu mudzatuluka ndi kulumphalumpha ngati ana angʼombe amene atulutsidwa mʼkhola. 3 Tsiku limenelo inu mudzapondereza anthu oyipa; adzakhala phulusa ku mapazi anu pa tsiku limene Ine ndidzachite zinthu zimenezi,” akutero Yehova Wamphamvuzonse.
4 Kumbukirani zophunzitsa za mtumiki wanga Mose, malamulo ndi malangizo amene ndinamupatsa pa Horebu kuti awuze Aisraeli onse.
5 “Taonani, ndidzakutumizirani mneneri Eliya lisanafike tsiku lalikulu ndi loopsa la Yehova. 6 Iye adzabweza mitima ya makolo kwa ana awo, ndi mitima ya ana kwa makolo awo. Kupanda kutero ndidzabwera kudzakantha dziko lanu ndi temberero.”
Malachi 4
New International Version
Judgment and Covenant Renewal
4 [a]“Surely the day is coming;(A) it will burn like a furnace.(B) All the arrogant(C) and every evildoer will be stubble,(D) and the day that is coming will set them on fire,(E)” says the Lord Almighty. “Not a root or a branch(F) will be left to them. 2 But for you who revere my name,(G) the sun of righteousness(H) will rise with healing(I) in its rays. And you will go out and frolic(J) like well-fed calves. 3 Then you will trample(K) on the wicked; they will be ashes(L) under the soles of your feet on the day when I act,” says the Lord Almighty.
4 “Remember the law(M) of my servant Moses, the decrees and laws I gave him at Horeb(N) for all Israel.(O)
5 “See, I will send the prophet Elijah(P) to you before that great and dreadful day of the Lord comes.(Q) 6 He will turn the hearts of the parents to their children,(R) and the hearts of the children to their parents; or else I will come and strike(S) the land with total destruction.”(T)
Footnotes
- Malachi 4:1 In Hebrew texts 4:1-6 is numbered 3:19-24.
Malachi 4
King James Version
4 For, behold, the day cometh, that shall burn as an oven; and all the proud, yea, and all that do wickedly, shall be stubble: and the day that cometh shall burn them up, saith the Lord of hosts, that it shall leave them neither root nor branch.
2 But unto you that fear my name shall the Sun of righteousness arise with healing in his wings; and ye shall go forth, and grow up as calves of the stall.
3 And ye shall tread down the wicked; for they shall be ashes under the soles of your feet in the day that I shall do this, saith the Lord of hosts.
4 Remember ye the law of Moses my servant, which I commanded unto him in Horeb for all Israel, with the statutes and judgments.
5 Behold, I will send you Elijah the prophet before the coming of the great and dreadful day of the Lord:
6 And he shall turn the heart of the fathers to the children, and the heart of the children to their fathers, lest I come and smite the earth with a curse.
The Word of God in Contemporary Chichewa Copyright © 2002, 2016 by Biblica, Inc.® Used by permission of Biblica, Inc.® All rights reserved worldwide. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Mwini © 2002, 2016 ndi Biblica, Inc.® Kugwiritsa ntchito mwachilolezo. Umwini ndi otetezedwa pa dziko lonse.
Holy Bible, New International Version®, NIV® Copyright ©1973, 1978, 1984, 2011 by Biblica, Inc.® Used by permission. All rights reserved worldwide.
NIV Reverse Interlinear Bible: English to Hebrew and English to Greek. Copyright © 2019 by Zondervan.