Add parallel Print Page Options

Tsiku la Yehova

Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Ndithu tsiku likubwera; lidzayaka ngati ngʼanjo. Anthu onse odzikuza, ndi aliyense ochita zoyipa adzapsa ngati chiputu, ndipo pa tsiku limene likubweralo adzapserera ndi moto. Sipadzatsalira muzu kapena nthambi. Koma inu amene mumaopa dzina langa, dzuwa lachilungamo lidzakutulukirani lili ndi kuwala kokuchiritsani. Ndipo inu mudzatuluka ndi kulumphalumpha ngati ana angʼombe amene atulutsidwa mʼkhola. Tsiku limenelo inu mudzapondereza anthu oyipa; adzakhala phulusa ku mapazi anu pa tsiku limene Ine ndidzachite zinthu zimenezi,” akutero Yehova Wamphamvuzonse.

Kumbukirani zophunzitsa za mtumiki wanga Mose, malamulo ndi malangizo amene ndinamupatsa pa Horebu kuti awuze Aisraeli onse.

“Taonani, ndidzakutumizirani mneneri Eliya lisanafike tsiku lalikulu ndi loopsa la Yehova. Iye adzabweza mitima ya makolo kwa ana awo, ndi mitima ya ana kwa makolo awo. Kupanda kutero ndidzabwera kudzakantha dziko lanu ndi temberero.”

Judgment and Covenant Renewal

[a]“Surely the day is coming;(A) it will burn like a furnace.(B) All the arrogant(C) and every evildoer will be stubble,(D) and the day that is coming will set them on fire,(E)” says the Lord Almighty. “Not a root or a branch(F) will be left to them. But for you who revere my name,(G) the sun of righteousness(H) will rise with healing(I) in its rays. And you will go out and frolic(J) like well-fed calves. Then you will trample(K) on the wicked; they will be ashes(L) under the soles of your feet on the day when I act,” says the Lord Almighty.

“Remember the law(M) of my servant Moses, the decrees and laws I gave him at Horeb(N) for all Israel.(O)

“See, I will send the prophet Elijah(P) to you before that great and dreadful day of the Lord comes.(Q) He will turn the hearts of the parents to their children,(R) and the hearts of the children to their parents; or else I will come and strike(S) the land with total destruction.”(T)

Footnotes

  1. Malachi 4:1 In Hebrew texts 4:1-6 is numbered 3:19-24.

For, behold, the day cometh, that shall burn as an oven; and all the proud, yea, and all that do wickedly, shall be stubble: and the day that cometh shall burn them up, saith the Lord of hosts, that it shall leave them neither root nor branch.

But unto you that fear my name shall the Sun of righteousness arise with healing in his wings; and ye shall go forth, and grow up as calves of the stall.

And ye shall tread down the wicked; for they shall be ashes under the soles of your feet in the day that I shall do this, saith the Lord of hosts.

Remember ye the law of Moses my servant, which I commanded unto him in Horeb for all Israel, with the statutes and judgments.

Behold, I will send you Elijah the prophet before the coming of the great and dreadful day of the Lord:

And he shall turn the heart of the fathers to the children, and the heart of the children to their fathers, lest I come and smite the earth with a curse.