Add parallel Print Page Options

Fuko la Levi

Ana a Levi anali awa:

Geresoni, Kohati ndi Merari.

Ana a Kohati anali awa:

Amramu, Izihari, Hebroni ndi Uzieli.

Ana a Amramu anali awa:

Aaroni, Mose ndi Miriamu.

Ana a Aaroni anali awa:

Nadabu, Abihu, Eliezara ndi Itamara

Eliezara anabereka Finehasi,

Finehasi anabereka Abisuwa,

Abisuwa anabereka Buki,

Buki anabereka Uzi.

Uzi anabereka Zerahiya,

Zerahiya anabereka Merayoti,

Merayoti anabereka Amariya,

Amariya anabereka Ahitubi.

Ahitubi anabereka Zadoki,

Zadoki anabereka Ahimaazi.

Ahimaazi anabereka Azariya,

Azariya anabereka Yohanani,

10 Yohanani anabereka Azariya (uyu ndi amene anatumikira monga wansembe mʼNyumba ya Mulungu imene Solomoni anamanga mu Yerusalemu),

11 Azariya anabereka Amariya,

Amariya anabereka Ahitubi,

12 Ahitubi anabereka Zadoki,

Zadoki anabereka Salumu,

13 Salumu anabereka Hilikiya,

Hilikiya anabereka Azariya,

14 Azariya anabereka Seraya,

ndipo Seraya anabereka Yehozadaki.

15 Yehozadaki anagwidwa ukapolo pamene Yehova analola Nebukadinezara kuti agwire ukapolo Yuda ndi Yerusalemu.

16 Ana a Levi anali awa:

Geresomu, Kohati ndi Merari.

17 Mayina a ana a Geresomu ndi awa:

Libini ndi Simei.

18 Ana a Kohati anali awa:

Amramu, Izihari, Hebroni ndi Uzieli.

19 Ana a Merari anali awa:

Mahili ndi Musi.

Mayina a mabanja a fuko la Levi olembedwa potsata makolo awo ndi awa:

20 Ana a Geresomu ndi awa:

Libini, Yehati,

Zima, 21 Yowa,

Ido, Zera

ndi Yeaterai.

22 Zidzukulu za Kohati ndi izi:

Aminadabu, Kora,

Asiri, 23 Elikana,

Ebiyasafu, Asiri,

24 Tahati, Urieli,

Uziya ndi Sauli.

25 Zidzukulu za Elikana ndi izi:

Amasai, Ahimoti,

26 Elikana, Zofai,

Nahati, 27 Eliabu,

Yerohamu, Elikana

ndi Samueli.

28 Ana a Samueli ndi awa:

Mwana wake woyamba anali Yoweli,

wachiwiri anali Abiya.

29 Zidzukulu za Merari ndi izi:

Mahili, Libini,

Simei, Uza,

30 Simea, Hagiya

ndi Asaya.

Oyimba mʼNyumba ya Mulungu

31 Awa ndi anthu amene Davide anawayika kuti aziyangʼanira mayimbidwe mʼNyumba ya Yehova, Bokosi la Chipangano litabwera kudzakhala mʼmenemo. 32 Iwo ankatumikira akuyimba nyimbo pa khomo la malo opatulika, tenti ya msonkhano, mpaka Solomoni atamanga Nyumba ya Yehova mu Yerusalemu. Iwo ankagwira ntchito zawo potsata malamulo amene anawapatsa.

33 Mayina a anthuwo, pamodzi ndi ana awo, anali awa:

Ochokera ku banja la Kohati:

Hemani, katswiri woyimba,

anali mwana wa Yoweli, mwana wa Samueli,

34 mwana wa Elikana, mwana wa Yerohamu,

mwana wa Elieli, mwana wa Towa,

35 mwana wa Zufi, mwana wa Elikana,

mwana wa Mahati, mwana wa Amasai,

36 mwana wa Elikana, mwana wa Yoweli,

mwana wa Azariya, mwana wa Zefaniya,

37 mwana wa Tahati, mwana wa Asiri,

mwana wa Ebiyasafu, mwana wa Kora,

38 mwana wa Izihari, mwana wa Kohati,

mwana wa Levi, mwana wa Israeli;

39 ndi Asafu mʼbale wake, amene ankatumikira ku dzanja lake lamanja:

Asafu anali mwana wa Berekiya, mwana wa Simea,

40 mwana wa Mikayeli, mwana wa Baaseya,

mwana wa Malikiya, 41 mwana wa Etini,

mwana wa Zera, mwana wa Adaya,

42 mwana wa Etani, mwana wa Zima,

mwana Simei, 43 mwana wa Yahati,

mwana wa Geresomu, mwana wa Levi;

44 ndipo abale awo ena anali a banja la Merari amene amatumikira ku dzanja lake lamanzere:

Etani anali mwana wa Kisi, mwana wa Abidi,

mwana wa Maluki, 45 mwana wa Hasabiya,

mwana wa Amaziya, mwana wa Hilikiya,

46 mwana wa Amizi, mwana wa Bani,

mwana wa Semeri, 47 mwana wa Mahili,

mwana wa Musi, mwana wa Merari,

mwana wa Levi.

48 Abale awo Alevi anapatsidwa ntchito zina zonse ku malo opatulika ku nyumba ya Mulungu. 49 Koma Aaroni ndi zidzukulu zake anali amene amapereka nsembe pa guwa lansembe zopsereza ndi pa guwa lansembe zofukiza pamodzi ndi zonse zimene zimachitika ku malo opatulika kwambiri, kuchita mwambo wopepesera Israeli, potsata zonse zimene Mose mtumiki wa Mulungu anawalamulira.

50 Ana a Aaroni ndi zidzukulu zake anali awa:

Eliezara, Finehasi,

Abisuwa, 51 Buki,

Uzi, Zerahiya,

52 Merayoti, Amariya,

Ahitubi, 53 Zadoki

ndi Ahimaazi.

54 Malo amene iwo anapatsidwa kuti likhale dziko lawo ndi awa: (Malowa anapatsidwa kwa zidzukulu za Aaroni zimene zinali za banja la Kohati, chifukwa malo oyamba kugawidwa anali awo).

55 Iwo anapatsidwa Hebroni mʼdziko la Yuda ndi madera odyetsera ziweto ozungulira malowa. 56 Koma minda ndi midzi yozungulira mzindawo zinapatsidwa kwa Kalebe mwana wa Yefune.

57 Kotero zidzukulu za Aaroni zinapatsidwa Hebroni (mzinda wopulumukirako), ndi Libina, Yatiri, Esitemowa, 58 Hileni, Debri, 59 Asani, Yuta ndi Beti-Semesi pamodzi ndi madera odyetsera ziweto ozungulira malowa. 60 Ndipo ku fuko la Benjamini anapatsidwa Gibiyoni, Geba, Alemeti ndi Anatoti, pamodzi ndi madera odyetsera ziweto ozungulira malowa.

Mizinda imene anapatsidwa ku banja la Kohati onse pamodzi inalipo 13.

61 Zidzukulu zotsala za Kohati anazigawira midzi khumi kuchokera ku mabanja a fuko la theka la Manase.

62 Zidzukulu za Geresomu banja ndi banja zinapatsidwa mizinda 13 kuchokera ku mafuko a Isakara, Aseri ndi Nafutali, ndi gawo lina la fuko la Manase limene lili ku Basani.

63 Zidzukulu za Merari banja ndi banja zinapatsidwa mizinda khumi ndi iwiri kuchokera ku mafuko a Rubeni, Gadi ndi Zebuloni.

64 Kotero Aisraeli anapatsa Alevi mizindayi ndi madera a msipu ozungulira malowa. 65 Kuchokera ku mafuko a Yuda, Simeoni ndi Benjamini anawapatsa mizinda imene inawatchula kale mayina.

66 Mabanja ena a Kohati anapatsidwanso malo kuchokera ku fuko la Efereimu.

67 Kuchokera ku dziko lamapiri la Efereimu anapatsidwa Sekemu (mzinda wopulumukirako) ndi Gezeri, 68 Yokineamu, Beti-Horoni, 69 Ayaloni ndi Gati-Rimoni, pamodzi ndi madera odyetsera ziweto ozungulira.

70 Ndipo kuchokera ku theka la fuko la Manase, Aisraeli anapereka Aneri ndi Bileamu pamodzi ndi madera odyetsera ziweto kwa mabanja ena onse a Kohati.

71 Ageresomu analandira malo awa:

Kuchokera ku theka la fuko la Manase,

analandira Golani ku Basani ndiponso Asiteroti, ndi malo awo odyetsera ziweto;

72 Kuchokera ku fuko la Isakara

analandira Kedesi, Daberati, 73 Ramoti ndi Anemu, pamodzi ndi malo ake odyetsera ziweto;

74 kuchokera ku fuko la Aseri

analandira Masala, Abidoni, 75 Hukoki ndi Rehobu, pamodzi ndi malo ake odyetsera ziweto;

76 ndipo kuchokera ku fuko la Nafutali

analandira Kedesi ku Galileya, Hamoni ndi Kiriyataimu, pamodzi ndi malo ake odyetsera ziweto.

77 Amerari (Alevi ena onse) analandira madera awa:

kuchokera ku fuko la Zebuloni,

iwo analandira Yokineamu, Karita, Rimono ndi Tabori, pamodzi ndi malo ake odyetsera ziweto;

78 Kuchokera ku fuko la Rubeni kutsidya kwa Yorodani, kummawa kwa Yeriko,

analandira Bezeri ku chipululu, Yaza, 79 Kedemoti ndi Mefaati, pamodzi ndi malo ake odyetsera ziweto;

80 ndipo kuchokera ku fuko la Gadi

analandira Ramoti ku Giliyadi, Mahanaimu, 81 Hesiboni ndi Yazeri, pamodzi ndi malo ake odyetsera ziweto.

Levi

[a]The sons of Levi:(A)

Gershon, Kohath and Merari.

The sons of Kohath:

Amram, Izhar, Hebron and Uzziel.(B)

The children of Amram:

Aaron, Moses and Miriam.(C)

The sons of Aaron:

Nadab, Abihu,(D) Eleazar(E) and Ithamar.(F)

Eleazar was the father of Phinehas,(G)

Phinehas the father of Abishua,

Abishua the father of Bukki,

Bukki the father of Uzzi,

Uzzi the father of Zerahiah,

Zerahiah the father of Meraioth,

Meraioth the father of Amariah,

Amariah the father of Ahitub,

Ahitub the father of Zadok,(H)

Zadok the father of Ahimaaz,

Ahimaaz the father of Azariah,

Azariah the father of Johanan,

10 Johanan the father of Azariah(I) (it was he who served as priest in the temple Solomon built in Jerusalem),

11 Azariah the father of Amariah,

Amariah the father of Ahitub,

12 Ahitub the father of Zadok,

Zadok the father of Shallum,

13 Shallum the father of Hilkiah,(J)

Hilkiah the father of Azariah,

14 Azariah the father of Seraiah,(K)

and Seraiah the father of Jozadak.[b]

15 Jozadak(L) was deported when the Lord sent Judah and Jerusalem into exile by the hand of Nebuchadnezzar.

16 The sons of Levi:(M)

Gershon,[c] Kohath and Merari.(N)

17 These are the names of the sons of Gershon:

Libni and Shimei.(O)

18 The sons of Kohath:

Amram, Izhar, Hebron and Uzziel.(P)

19 The sons of Merari:(Q)

Mahli and Mushi.(R)

These are the clans of the Levites listed according to their fathers:

20 Of Gershon:

Libni his son, Jahath his son,

Zimmah his son, 21 Joah his son,

Iddo his son, Zerah his son

and Jeatherai his son.

22 The descendants of Kohath:

Amminadab his son, Korah(S) his son,

Assir his son, 23 Elkanah his son,

Ebiasaph his son, Assir his son,

24 Tahath his son, Uriel(T) his son,

Uzziah his son and Shaul his son.

25 The descendants of Elkanah:

Amasai, Ahimoth,

26 Elkanah his son,[d] Zophai his son,

Nahath his son, 27 Eliab his son,

Jeroham his son, Elkanah(U) his son

and Samuel(V) his son.[e]

28 The sons of Samuel:

Joel[f](W) the firstborn

and Abijah the second son.

29 The descendants of Merari:

Mahli, Libni his son,

Shimei his son, Uzzah his son,

30 Shimea his son, Haggiah his son

and Asaiah his son.

The Temple Musicians(X)

31 These are the men(Y) David put in charge of the music(Z) in the house of the Lord after the ark came to rest there. 32 They ministered with music before the tabernacle, the tent of meeting, until Solomon built the temple of the Lord in Jerusalem. They performed their duties according to the regulations laid down for them.

33 Here are the men who served, together with their sons:

From the Kohathites:

Heman,(AA) the musician,

the son of Joel,(AB) the son of Samuel,

34 the son of Elkanah,(AC) the son of Jeroham,

the son of Eliel, the son of Toah,

35 the son of Zuph, the son of Elkanah,

the son of Mahath, the son of Amasai,

36 the son of Elkanah, the son of Joel,

the son of Azariah, the son of Zephaniah,

37 the son of Tahath, the son of Assir,

the son of Ebiasaph, the son of Korah,(AD)

38 the son of Izhar,(AE) the son of Kohath,

the son of Levi, the son of Israel;

39 and Heman’s associate Asaph,(AF) who served at his right hand:

Asaph son of Berekiah, the son of Shimea,(AG)

40 the son of Michael, the son of Baaseiah,[g]

the son of Malkijah, 41 the son of Ethni,

the son of Zerah, the son of Adaiah,

42 the son of Ethan, the son of Zimmah,

the son of Shimei, 43 the son of Jahath,

the son of Gershon, the son of Levi;

44 and from their associates, the Merarites,(AH) at his left hand:

Ethan son of Kishi, the son of Abdi,

the son of Malluk, 45 the son of Hashabiah,

the son of Amaziah, the son of Hilkiah,

46 the son of Amzi, the son of Bani,

the son of Shemer, 47 the son of Mahli,

the son of Mushi, the son of Merari,

the son of Levi.

48 Their fellow Levites(AI) were assigned to all the other duties of the tabernacle, the house of God. 49 But Aaron and his descendants were the ones who presented offerings on the altar(AJ) of burnt offering and on the altar of incense(AK) in connection with all that was done in the Most Holy Place, making atonement for Israel, in accordance with all that Moses the servant of God had commanded.

50 These were the descendants of Aaron:

Eleazar his son, Phinehas his son,

Abishua his son, 51 Bukki his son,

Uzzi his son, Zerahiah his son,

52 Meraioth his son, Amariah his son,

Ahitub his son, 53 Zadok(AL) his son

and Ahimaaz his son.

54 These were the locations of their settlements(AM) allotted as their territory (they were assigned to the descendants of Aaron who were from the Kohathite clan, because the first lot was for them):

55 They were given Hebron in Judah with its surrounding pasturelands. 56 But the fields and villages around the city were given to Caleb son of Jephunneh.(AN)

57 So the descendants of Aaron were given Hebron (a city of refuge), and Libnah,[h](AO) Jattir,(AP) Eshtemoa, 58 Hilen, Debir,(AQ) 59 Ashan,(AR) Juttah[i] and Beth Shemesh, together with their pasturelands. 60 And from the tribe of Benjamin they were given Gibeon,[j] Geba, Alemeth and Anathoth,(AS) together with their pasturelands.

The total number of towns distributed among the Kohathite clans came to thirteen.

61 The rest of Kohath’s descendants were allotted ten towns from the clans of half the tribe of Manasseh.

62 The descendants of Gershon, clan by clan, were allotted thirteen towns from the tribes of Issachar, Asher and Naphtali, and from the part of the tribe of Manasseh that is in Bashan.

63 The descendants of Merari, clan by clan, were allotted twelve towns from the tribes of Reuben, Gad and Zebulun.

64 So the Israelites gave the Levites these towns(AT) and their pasturelands. 65 From the tribes of Judah, Simeon and Benjamin they allotted the previously named towns.

66 Some of the Kohathite clans were given as their territory towns from the tribe of Ephraim.

67 In the hill country of Ephraim they were given Shechem (a city of refuge), and Gezer,[k](AU) 68 Jokmeam,(AV) Beth Horon,(AW) 69 Aijalon(AX) and Gath Rimmon,(AY) together with their pasturelands.

70 And from half the tribe of Manasseh the Israelites gave Aner and Bileam, together with their pasturelands, to the rest of the Kohathite clans.

71 The Gershonites(AZ) received the following:

From the clan of the half-tribe of Manasseh

they received Golan in Bashan(BA) and also Ashtaroth, together with their pasturelands;

72 from the tribe of Issachar

they received Kedesh, Daberath,(BB) 73 Ramoth and Anem, together with their pasturelands;

74 from the tribe of Asher

they received Mashal, Abdon,(BC) 75 Hukok(BD) and Rehob,(BE) together with their pasturelands;

76 and from the tribe of Naphtali

they received Kedesh in Galilee, Hammon(BF) and Kiriathaim,(BG) together with their pasturelands.

77 The Merarites (the rest of the Levites) received the following:

From the tribe of Zebulun

they received Jokneam, Kartah,[l] Rimmono and Tabor, together with their pasturelands;

78 from the tribe of Reuben across the Jordan east of Jericho

they received Bezer(BH) in the wilderness, Jahzah, 79 Kedemoth(BI) and Mephaath, together with their pasturelands;

80 and from the tribe of Gad

they received Ramoth in Gilead,(BJ) Mahanaim,(BK) 81 Heshbon and Jazer,(BL) together with their pasturelands.(BM)

Footnotes

  1. 1 Chronicles 6:1 In Hebrew texts 6:1-15 is numbered 5:27-41, and 6:16-81 is numbered 6:1-66.
  2. 1 Chronicles 6:14 Hebrew Jehozadak, a variant of Jozadak; also in verse 15
  3. 1 Chronicles 6:16 Hebrew Gershom, a variant of Gershon; also in verses 17, 20, 43, 62 and 71
  4. 1 Chronicles 6:26 Some Hebrew manuscripts, Septuagint and Syriac; most Hebrew manuscripts Ahimoth 26 and Elkanah. The sons of Elkanah:
  5. 1 Chronicles 6:27 Some Septuagint manuscripts (see also 1 Samuel 1:19,20 and 1 Chron. 6:33,34); Hebrew does not have and Samuel his son.
  6. 1 Chronicles 6:28 Some Septuagint manuscripts and Syriac (see also 1 Samuel 8:2 and 1 Chron. 6:33); Hebrew does not have Joel.
  7. 1 Chronicles 6:40 Most Hebrew manuscripts; some Hebrew manuscripts, one Septuagint manuscript and Syriac Maaseiah
  8. 1 Chronicles 6:57 See Joshua 21:13; Hebrew given the cities of refuge: Hebron, Libnah.
  9. 1 Chronicles 6:59 Syriac (see also Septuagint and Joshua 21:16); Hebrew does not have Juttah.
  10. 1 Chronicles 6:60 See Joshua 21:17; Hebrew does not have Gibeon.
  11. 1 Chronicles 6:67 See Joshua 21:21; Hebrew given the cities of refuge: Shechem, Gezer.
  12. 1 Chronicles 6:77 See Septuagint and Joshua 21:34; Hebrew does not have Jokneam, Kartah.